Psalms 69:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzatamanda dzina la Mulungu pomuimbira nyimbo, ndidzalalika ukulu wake pomuthokoza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzalemekeza dzina la Mulungu ndi kuliimbira, ndipo ndidzambukitsa ndi kumyamika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndidzatamanda dzina la Mulungu mʼnyimbo, ndidzalemekeza Iye ndi chiyamiko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzalemekeza dzina la Mulungu ndi kuliyimbira, Ndipo ndidzambukitsa ndi kumyamika.