Psalms 7:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonadi, munthu woipa amalingalira zoipa zokhazokha nthaŵi zonse, ntchito yake ndi kunyenga ndi kuvutitsa anthu ena basi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ali m'chikuta cha zopanda pake; anaima ndi chovuta, nabala bodza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse. Zochita zake ndi zosokoneza ndi zovutitsa anthu ena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ali m'cikuta ca zopanda pace; Anaima ndi cobvuta, nabala bodza.