Psalms 71:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa panga pakutamanda Inu, pakulalika ulemerero wanu tsiku lonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kamwa mwanga mudzadzala lemekezo lanu, ndi ulemu wanu tsiku lonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kamwa mwanga mudzadzala lemekezo lanu, Ndi ulemu wanu tsiku lonse.