Psalms 74:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adadulamo zonse, monga momwe anthu amadulira mitengo m'nkhalango.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anaoneka ngati osamula nkhwangwa kunkhalango.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo kuti adule mitengo mʼnkhalango.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anaoneka ngati osamula nkhwangwa kunkhalango.