Psalms 86:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Ambuye ndinu abwino, ndipo mumakhululukira anthu anu. Chikondi chanu chosasinthika ndi chachikulu kwa onse amene amakupembedzani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu Ambuye, ndinu wokhululuka ndi wabwino, wodzaza ndi chikondi kwa onse amene amayitana Inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti fnu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, Ndi wa cifundo cocurukira onse akuitana Inu.