Psalms 88:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, chifukwa chiyani mukunditaya? Chifukwa chiyani mukundibisira nkhope yanu?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova mutayiranji moyo wanga? Ndi kundibisira nkhope yanu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu Yehova nʼchifukwa chiyani mukundikana ndi kundibisira nkhope yanu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova mutayiranji moyo wanga? Ndi kundibisira nkhope yanu?