Psalms 90:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono tiphunzitseni kuŵerenga masiku athu, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, Kuti tikhale nao mtima wanzeru.