Revelation 11:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo anthu onse okhala pa dziko lapansi adzakondwera nazo zimenezi. Adzachita chikondwerero ndi kutumizirana mphatso, chifukwa aneneri aŵiriŵa ankaŵasautsa kwambiri anthu okhala pa dziko lapansiwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo akukhala padziko adzakondwerera, nasekerera, nadzatumizirana mitulo; popeza aneneri awa awiri anazunza iwo akukhala padziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu okhala pa dziko lapansi adzasangalala nazo zimenezi. Adzachita chikondwerero ndi kutumizirana mphatso, chifukwa aneneri awiri amenewa ankasautsa anthu okhala pa dziko lapansi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo akukhala padziko adzakondwerera, nasekerera, nadzatumizirana mitulo; popeza aneneri awa awiri anazunza iwo akukhala padziko.