Revelation 11:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Akuluakulu 24 aja okhala pa mipando yao yachifumu pamaso pa Mulungu, adadzigwetsa chafufumimba napembedza Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo akulu makumi awiri mphambu anai akukhala pamaso pa Mulungu pa mipando yachifumu yao, anagwa nkhope yao pansi nalambira Mulungu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo akuluakulu 24 aja okhala pa mipando yawo yaufumu pamaso pa Mulungu, anadzigwetsa chafufumimba napembedza Mulungu
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo akulu makumi awiri mphambu anai akukhala pamaso pa Mulungu pa mipando yacifumu yao, anagwa nkhope yao pansi nalambira Mulungu,