Revelation 11:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adati, “Ambuye Mulungu, Mphambe, Inu amene mulipo ndipo munaliponso kale, tikukuyamikani chifukwa mwaonetsa mphamvu yanu yaikulu, ndipo mwayamba kukhazikitsa ufumu wanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nati, Tikuyamikani, Ambuye Mulungu, Wamphamvuyonse, amene muli, nimunali; popeza mwadzitengera mphamvu yanu yaikulu, ndipo mwachita ufumu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anati, “Ife tikuyamika Inu Ambuye Mulungu Wamphamvuzonse, amene mulipo ndipo munalipo, chifukwa mwaonetsa mphamvu yanu yayikulu, ndipo mwayamba kulamulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nati, Tikuyamikani, Ambuye Mulungu, Wamphamvuyonse, amene muli, nimunali; popeza mwadzitengera mphamvu yanu yaikuru, ndipo mwacita ufumu.