Revelation 11:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma bwalo la kunja kwa Nyumbayo ulisiye, osaliyesa. Bwalo limeneli lidapatsidwa kwa anthu akunja, ndipo iwowo adzaupondereza Mzinda woyerawo pa miyezi 42.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo bwalo la kunja kwa Kachisi ulisiye padera, osaliyesa; pakuti adapatsa ilo kwa amitundu; ndipo mzinda wopatulika adzaupondereza miyezi makumi anai mphambu iwiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma bwalo lakunja ulisiye, usaliyeze chifukwa linaperekedwa kwa a mitundu ina. Iwo adzawupondereza mzinda woyerawo kwa miyezi 42.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo bwalo la kunja kwa Kacisi ulisiye padera, osaliyesa; pakuti adapatsa ilo kwa amitundu; ndipo mzinda wopatulika adzaupondereza miyezi makumi anai mphambu iwiri.