Revelation 14:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kenaka padafikanso mngelo wina wachitatu, wotsatana ndi aŵiri ena aja. Mokweza mau adati, “Aliyense wopembedza chilombo chija ndi fano lake, ndi kulembedwa chizindikiro pa mphumi kapena pa dzanja,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anawatsata mngelo wina, wachitatu, nanena ndi mau akulu, Ngati wina alambira chilombocho, ndi fano lake, nalandira lemba pamphumi pake, kapena pa dzanja lake
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mngelo wachitatu anatsatana nawo ndi mawu ofuwula anati, “Ngati wina apembedza chirombo chija ndi fano lake ndi kulembedwa chizindikiro pa mphumi kapena pa dzanja,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anawatsata mngelo wina, wacitatu, nanena ndi mau akuru, Ngati wina alambira ciromboco, ndi fane lace, nalandira lembapamphumi pace, kapena pa dzanja lace,