Revelation 16:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti iwo aja adakhetsa magazi a anthu a Mulungu, ndi a aneneri, nchifukwa chake mwaŵapatsa magazi kuti amwe. Zimenezi ndi zimene zikuŵayenera.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
popeza anatsanulira mwazi wa oyera mtima, ndi wa aneneri, ndipo mudawapatsa mwazi amwe; ayenera iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pakuti iwo anakhetsa magazi a oyera anu ndi aneneri anu, nʼchifukwa chake mwawapatsa magazi kuti amwe, zomwe zikuwayenera.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
popeza anatsanulira mwazi wa oyera mtima, ndi wa aneneri, ndipo mudawapatsa mwazi amwe; ayenera iwo.