Revelation 18:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kondwerani inu, Dziko la Kumwamba, chifukwa cha kuwonongeka kwake. Kondwerani inu, anthu a Mulungu, inu atumwi, ndi inunso aneneri. Pakuti Mulungu pakuulanga mzindawo, wautsutsa kuti ndi wolakwa pa zimene udakuchitani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kondwera pa iye, m'mwamba iwe, ndi oyera mtima, ndi atumwi, ndi aneneri inu; chifukwa Mulungu anauweruzira kuweruzidwa kwanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kondwerani chifukwa cha iye inu kumwamba! Kondwerani oyera mtima ndi atumwi ndi aneneri! Mulungu wamuweruza iye monga momwe anakuchitirani inu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kondwera pa iye, m'mwamba iwe, ndi oyera mtima, ndi atumwi, ndi aneneri inu; cifukwa Mulungu anauweruzira kuweruzidwa kwanu.