Revelation 18:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mu mzinda umenewo mudapezeka magazi a aneneri, ndi a anthu a Mulungu, ndi a anthu onse amene adaphedwa pa dziko lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo momwemo munapezedwa mwazi wa aneneri ndi oyera mtima, ndi onse amene anaphedwa padziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwa iye munapezeka magazi a aneneri ndi a oyera mtima, ndi onse amene anaphedwa pa dziko lapansi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo 3 momwemo munapezedwa mwazi wa aneneri ndi oyera mtima, ndi onse amene anaphedwa padziko.