Revelation 19:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye waloledwa kuvala zovala za nsalu yabafuta, yoŵala, yoombedwa bwino.” (Zovala zabafutazo zikutanthauza ntchito zabwino za anthu a Mulungu.)
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anampatsa iye avale bafuta wonyezimira woti mbu; pakuti bafuta ndiye zolungama za oyera mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wapatsidwa nsalu yoyera kwambiri, yowala ndi yosada kuti avale.” (Nsalu yoyera kwambiri ikuyimira ntchito zolungama za oyera mtima).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anampatsa iye abvale bafuta wonyezimira woti mbu; pakuti bafuta ndiye zolungama za oyera mtima.