Revelation 2:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komatu pokudzudzulirani palipo: ndi apa pakuti mwasiya chikondi chimene munkandikonda nacho poyamba paja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ndili nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya chikondi chako choyamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Komabe ndili ndi chotsutsana nawe: Wataya chikondi chako chapoyamba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ndiri nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya cikondi cako coyamba.