Revelation 22:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndine, Yohane, amene ndidamva ndi kuwona zimenezi. Ndipo nditazimva ndi kuziwona, ndidadzigwetsa ku mapazi a mngelo uja amene adandiwonetsa zimenezi. Ndidaati ndimpembedze,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ine Yohane ndine wakumva ndi wakupenya izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kupenya, ndinagwa pansi kulambira pa mapazi a mngelo wakundionetsa izo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine Yohane, ndine amene ndinamva ndi kuona zinthu izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kuona izi ndinagwa pansi kuti ndipembedze mngelo amene amandionetsa zimenezi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ine Yohane ndine wakumva ndi wakupenya izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kupenya, ndinagwa pansi kulambira pa mapazi a mngelo wakundionetsa izo.