Revelation 4:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi yomweyo ndidagwidwa ndi Mzimu Woyera. Kumwambako ndidaona mpando wachifumu, wina atakhalapo pampandopo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo ndinakhala mwa Mzimu; ndipo, taonani padaikika mpando wachifumu m'Mwamba ndi pa mpandowo padakhala wina;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi yomweyo ndinatengedwa ndi Mzimu Woyera, ndipo patsogolo panga ndinaona mpando waufumu wina atakhalapo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo ndinakhala mwa Mzimu; ndipo, taonani padaikika mpando wacifumu m'Mwamba ndi pa mpandowo padakhala wina;