Revelation 4:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando wachifumuyu, amene ali ndi moyo wamuyaya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene zamoyozo zipereka ulemerero ndi ulemu ndi uyamiko kwa Iye wakukhala pa mpando wachifumu, kwa Iye wakukhala ndi moyo kufikira nthawi za nthawi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene zamoyozo zipereka ulemerero ndi ulemu ndi uyamiko kwa iye wakukhala pa mpando wacifumu, kwa iye wakukhala ndi moyo kufikira nthawi za nthawi,