Revelation 9:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dzombelo lidalamulidwa kuti lisaononge udzu wa pa dziko lapansi, kapena chomera chilichonse, kapena mtengo uliwonse. Lidaloledwa kungoononga anthu opanda chizindikiro cha Mulungu chija pamphumi pao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ananena kwa ilo kuti lisaipse udzu wa padziko, kapena chabiriwiri chilichonse, kapena mtengo uliwonse, koma anthu amene alibe chizindikiro cha Mulungu pamphumi pao ndiwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Dzombelo linalamulidwa kuti lisawononge udzu wa pa dziko lapansi, kapena chomera chilichonse, kapena mtengo uliwonse, koma anthu okhawo amene analibe chizindikiro cha Mulungu pa mphumi zawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ananena kwa ilo kuti lisaipse udzu wa padziko, kapena cabiriwiri ciri conse, kapena mtengo uli wonse, koma anthu amene alibe cizindikilo ca Mulungu pamphumi pao ndiwo.