Romans 1:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo amadziyesa anzeru, koma chikhalirecho ndi opusa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakunena kuti ali anzeru, anapusa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale ankadzitama kuti ndi anzeru, anasanduka opusa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakunena kuti ali anzeru, anapusa;