Romans 10:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero munthu amakhulupirira chifukwa cha zimene wamva, ndipo zimene wamvazo zimachokera ku zolalika za Khristu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chomwecho chikhulupiriro chidza ndi mbiri, ndi mbiri idza mwa mau a Khristu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero, chikhulupiriro chimabwera pamene timva uthenga ndipo uthenga umamveka kuchokera ku mawu a Khristu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Comweco cikhulupiriro cidza ndi mbiri, ndi mbiri idza mwa mau a Kristu.