Romans 12:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzikondana kwenikweni monga abale, ndipo muzichita ngati kupikisana poonetsana ulemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukondane kwathunthu monga abale. Lemekezanani wina ndi mnzake kuposa inu eni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'cikondano ca anzanu wina ndi mnzace mukondane ndi cikondi ceni ceni; mutsogolerane ndi kucitira wina mnzace ulemu;