Romans 12:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzikondwa nawo amene akukondwa, muzilira nawo amene akulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kondwani nao iwo akukondwera; lirani nao akulira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kondwani pamodzi ndi amene akukondwa ndipo lirani ndi amene akulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kondwani nao iwo akukondwera; lirani nao akulira.