Romans 12:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati nkotheka, khalani ndi mtendere ndi anthu onse, monga momwe mungathere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati nʼkotheka, khalani mwamtendere ndi aliyense monga momwe mungathere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.