Romans 15:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono pokhala ndine wake wa Khristu Yesu, ndikunyadira ntchito imene ndikugwirira Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndili nacho chodzitamandira cha m'Khristu Yesu ndi zinthu za kwa Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho, ine ndikunyadira mwa Khristu Yesu potumikira Mulungu wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndiri naco codzitamandira ca m'Kristu Yesu ndi zinthu za kwa Mulungu.