Romans 15:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mundipempherere kuti Mulungu anditchinjirize, ndisagwe m'manja mwa anthu osakhulupirira am'Yudeya. Mupempherenso kuti anthu a Mulungu a ku Yerusalemu azilandire ndi manja aŵiri zoperekazi zimene ndatumidwa kuti ndikaŵapatse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti ndikapulumutsidwe kwa osamvera aja a ku Yudeya; ndi kuti utumiki wanga wa ku Yerusalemu ukhale wolandiridwa bwino ndi oyera mtima;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pempherani kuti ine ndilanditsidwe kwa osakhulupirira a ku Yudeya ndi kuti utumiki wanga mu Yerusalemu ukhale ovomerezeka ndi oyera mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti ndikapulumutsidwe kwa osamvera aja a ku Yudeya; ndi kuti utumiki wanga wa ku Yerusalemu ukhale wolandiridwa bwino ndi oyera mtima;