Romans 16:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mundiperekerenso moni kwa anthu amene amasonkhana ngati ampingo m'nyumba mwao. Moni kwa Epeneto, bwenzi langa lapamtima, amene ndi woyamba mu Asiya kukhulupirira Khristu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo mupereke moni kwa Mpingo wa Ambuye wa m'nyumba mwao. Moni kwa Epeneto wokondedwa wanga, ndiye chipatso choundukula cha Asiya cha kwa Khristu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Perekaninso moni kwa mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwawo. Perekani moni kwa mʼbale wanga wokondedwa Epeneto, amene ndi woyamba kukhulupirira Khristu mʼchigawo cha Asiya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo mulankhule Mpingo wa Ambuye wa m'nyumba mwao. Mulankhule Epeneto wokondedwa wanga, ndiye cipatso coundukula ca Asiya ca kwa Kristu,