Romans 16:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Moni kwa Urbano, mtumiki mnzathu pa ntchito ya Khristu, ndiponso kwa Stakisi, amene ndimamkonda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moni kwa Urbano wantchito mnzathu mwa Khristu, ndi Stakisi wokondedwa wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Perekani moni kwa Urbano, mtumiki mnzathu mwa Khristu ndi wokondedwa wanga Staku.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulankhule Urbano wanchito mnzathu mwa Kristu, ndi Staku wokondedwa wanga,