Romans 3:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Malembo akuti, “Palibe munthu wolungama, ai ndithu ndi mmodzi yemwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
monga kwalembedwa, Palibe mmodzi wolungama, inde palibe mmodzi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga kwalembedwa kuti, “Palibe munthu wolungama, inde palibe ndi mmodzi yemwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
monga kwalembedwa, Palibe mmodzi wolungama, inde palibe mmodzi;