Romans 3:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mpang'ono pomwe. Mulungu akadakhala wosalungama, akadatha bwanji kukhala woweruza anthu onse?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Msatero ai. Ngati kotero, Mulungu adzaweruza bwanji mlandu wa dziko lapansi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Ngati zikanakhala zotero, kodi Mulungu akanaweruza bwanji dziko lapansi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Msatero ai. Ngati kotero, Mulungu adzaweruza bwanji mlandu wa dziko lapansi?