Romans 4:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adakhulupirira ndithu kuti Mulungu angathe kuchita zimene adalonjeza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nakhazikikanso mumtima kuti, chimene Iye analonjeza, anali nayonso mphamvu yakuchichita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anatsimikiza mu mtima mwake kuti Mulungu anali ndi mphamvu yochita chomwe analonjeza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nakhazikikanso mumtima kuti, o cimene iye analonjeza, anali nayonso mphamvu yakucicita.