Romans 4:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a m'Malemboŵa onena kuti, “Mulungu adamuwona kuti ngwolungama,” sangonena za iye yekha ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ichi sichinalembedwa chifukwa cha iye yekhayekha, kuti chidawerengedwa kwa iye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu akuti, “chinatengedwa kwa iye” sanalembedwe chifukwa cha iye yekha,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ici sicinalembedwa cifukwa caiye yekha yekha, kuti cidawerengedwa kwa iye;