Romans 4:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akunenanso za ife amene tidzapezeka kuti ndife olungama pakukhulupirira Mulungu, amene adaukitsa Yesu Ambuye athu kwa akufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma chifukwa cha ifenso, kwa ife amene chidzawerengedwa kwa ife amene tikhulupirira Iye amene anaukitsa kwa akufa Yesu Ambuye wathu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
komanso chifukwa ife amene Mulungu adzatiyesa olungama, ife amene tikhulupirira mwa Iye amene anamuukitsa kwa akufa, Yesu Ambuye athu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma cifukwa ca ifenso, kwa ife amene cidzawerengedwa kwa ife amene tikhulupirira iye amene anaukitsa kwa akufa Yesu Ambuye wathu,