Romans 6:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono uchimo sudzakhalanso ndi mphamvu pa inu, pakuti chimene chimalamulira moyo wanu si Malamulo ai koma kukoma mtima kwa Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti uchimo sudzachita ufumu pa inu; popeza simuli a lamulo koma a chisomo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tchimo silidzakhalanso ndi mphamvu pa inu, chifukwa Malamulo sakulamulira moyo wanu koma chisomo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ucimo sudzacita ufumu pa inu; popeza simuli a lamulo koma a cisomo.