Romans 8:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mzimu Woyera mwiniwakeyo ndi amene amavomerezana ndi mitima yathu kutsimikiza kuti ndife ana a Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mzimu yekha achita umboni pamodzi ndi mzimu wathu, kuti tili ana a Mulungu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mzimu mwini amavomerezana ndi mzimu wathu kuti ife ndife ana a Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mzimu yekha acita umboni pamodzi ndi mzimu wathu, kuti tiri ana a Mulungu;