Romans 9:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Malembo akuti, “Yakobe ndidaamukonda, koma Esau ndidaadana naye.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inde monga kunalembedwa, Ndinakonda Yakobo, koma ndinamuda Esau.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga momwe kwalembedwa kuti, “Ine ndinakonda Yakobo, koma ndinamuda Esau.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inde monga kunalembedwa, Ndinakonda Yakobo, koma ndinamuda Esau.