Song of Solomon 2:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndili ngati duŵa la ku Saroni, ngati kakombo wam'zigwa. Mwamuna
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndine duwa lofiira la ku Saroni, ngakhale kakombo wa kuzigwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndine duwa la ku Saroni, duwa lokongola la ku zigwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndine duwa lofiira la ku Saroni, Ngakhale kakombo wa kuzigwa.