Song of Solomon 2:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wokondedwa wangayo ndi wangadi, ndipo ine ndine wake. Amadyetsa gulu lake la ziŵeto pakati pa akakombo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokondedwa wanga ndi wa ine, ine ndine wake: aweta zake pakati akakombo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Bwenzi langa ndi wangadi ndipo ine ndine wake; amadyetsa gulu lake la ziweto pakati pa maluwa okongola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokondedwa wanga ndi wa ine, ine ndine wace: Aweta zace pakati pa akakombo,