Song of Solomon 2:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tamvani liwu la wokondedwa wanga! Taonani akubwera, akulumphalumpha pa mapiri, akujoŵajoŵa pa zitunda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau a wokondedwa wanga mnyamatayo! Taona, adza, alikulumpha pamapiri, alikujidimuka pazitunda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tamverani bwenzi langa! Taonani! Uyu akubwera apayu, akulumphalumpha pa mapiri, akujowajowa pa zitunda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau a wokondedwa wanga mnyamatayo! Taona, adza, Alikulumpha pamapiri, alikujidimuka pazitunda.