Song of Solomon 3:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usiku uliwonse ndili gone pabedi panga ndinkangomufunafuna amene mtima wanga umamkonda. Ndidamufunafuna koma osampeza. Ndidamuitana, koma iye osandiyankha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usiku pamphasa panga ndinamfunafuna amene moyo wanga umkonda: Ndinamfunafuna, koma osampeza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usiku wonse ndili pa bedi langa ndinafunafuna amene mtima wanga umamukonda; ndinamufunafuna koma osamupeza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usiku pamphasa panga ndinamfunafuna amene moyo wanga umkonda: Ndinamfunafuna, koma osampeza.