Song of Solomon 3:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Milongoti yake adapanga yasiliva, kumbuyo kwake kunali kwagolide, pampando pake panali nsalu yofiirira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anapanga timilongoti take ndi siliva, cha pansi pake ndi golide, mpando wake ndi nsalu yofiirira, pakati pake panayalidwa za chikondi cha ana akazi a ku Yerusalemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Milongoti yake anayipanga yasiliva, kumbuyo kwake kwa golide. Mipando yake inakutidwa ndi nsalu yapepo, anakongoletsa mʼkati mwake ndi chikondi cha akazi a ku Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anapanga timilongoti tace ndi siliva, Ca pansi pace ndi golidi, mpando wace ndi nsaru yakuda, Pakati pace panayalidwa za cikondi ca ana akazi a ku Yerusalemu.