Song of Solomon 3:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndakupembani, pali mphoyo ndi nswala zakuthengo, chikondichi musachigwedeze kapena kuchiwutsa mpaka pamene chifunire ichocho. Mkazi
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikulumbirirani, ana akazi inu a ku Yerusalemu, pali mphoyo, ndi mbawala ya kuthengo, kuti musautse, ngakhale kugalamutsa chikondi, mpaka chikafuna mwini.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani pali gwape ndi mbawala yayikazi zakuthengo: Musachigwedeze chikondi kapena kuchiutsa mpaka pamene chifunire ichocho.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikulumbirirani, ana akazi inu a ku Yerusalemu, Pali mphoyo, ndi nswala ya kuthengo, Kuti musautse, ngakhale kugalamutsa cikondi, Mpaka cikafuna mwini.