Song of Solomon 3:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi nchiyaninso icho chikutulukira ku chipululucho ngati utsi watolotolo, chonunkhira mure ndi lubani, chokhala ndi zonunkhira zonse zogulitsa anthu amalonda?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndaniyu akwera kutuluka m'chipululu ngati utsi wa tolo, wonunkhira ndi mure ndi lubani, ndi zonunkhiritsa zonse za wogulitsa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ndani amene akubwera kuchokera ku chipululu ngati utsi watolotolo, wonunkhira mure ndi lubani, zopangidwa kuchokera ku zonunkhira zonse za anthu amalonda?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndaniyu akwera kuturuka m'cipululu ngati utsi wa tolo, Wonunkhira ndi nipa ndi mtanthanyerere, Ndi zonunkhiritsa zonse za wogulitsa?