Song of Solomon 3:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amenewo ndi machira a Solomoni. Pali ankhondo makumi asanu ndi limodzi, amuna anyonga a ku Israele operekeza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ndi machila a Solomoni; pazingapo amuna amphamvu makumi asanu ndi limodzi, a mwa ngwazi za Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ona! Chimenecho ndi chonyamulira Solomoni, choperekezedwa ndi asilikali 60, anthu amphamvu a ku Israeli,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ndi macila a Solomo; Pazingapo amuna amphamvu makumi asanu ndi limodzi, A mwa ngwazi za Israyeli.