Song of Solomon 3:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Onsewo agwira malupanga, ndipo ngodziŵa kumenya nkhondo, aliyense wavala lupanga pambali pake, kuti alimbane ndi aupandu usiku.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onsewo agwira lupanga, nazolowera nkhondo: Yense ali ndi lupanga lake pantchafu pake, chifukwa cha upandu wa usiku.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
onse atanyamula lupanga, onse odziwa bwino nkhondo, aliyense ali ndi lupanga pambali pake, kukonzekera zoopsa za usiku.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onsewo agwira lupanga, nazolowera nkhondo: Yense ali ndi lupanga lace pancafu pace, Cifukwa ca upandu wa usiku.