Song of Solomon 3:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mfumu Solomoni adadzipangira machira a matabwa a ku Lebanoni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Solomoni mfumu anadzipangira machila okhalamo tsonga ndi matabwa a ku Lebanoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu Solomoni anadzipangira chonyamulirachi; anachipanga ndi matabwa ochokera ku Lebanoni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Solomo mfumu anadzipangira macila okhalamo tsonga Ndi matabwa a ku Lebano.