Song of Solomon 7:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Khosi lako lili see ngati nsanja ya mnyanga wanjovu. Maso ako ali ngati maiŵe a ku Hesiboni, amene ali pafupi ndi chipata cha ku Batirabimu. Mphuno yako ikuwoneka ngati nsanja ya ku Lebanoni, yoyang'ana ku Damasiko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Khosi lako likunga nsanja yaminyanga; maso ako akunga matawale a ku Hesiboni, a pa chipata cha Batirabimu; mphuno yako ikunga nsanja ya ku Lebanoni imene iloza ku Damasiko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Khosi lako lili see! ngati nsanja ya mnyanga wa njovu. Maso ako ali ngati mayiwe a ku Hesiboni, amene ali pafupi ndi chipata cha Bati Rabimu. Mphuno yako ili ngati nsanja ya ku Lebanoni, yoyangʼana ku Damasiko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Khosi lako likunga nsanja yaminyanga; Maso ako akunga matawale a ku Hesiboni, A pa cipata ca Batirabimu; Mphuno yako ikunga nsanja ya ku Lebano Imene iloza ku Damasiko.