Song of Solomon 8:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndili ngati khoma, ndipo maŵere anga ali ngati nsanja zake. Tsono m'maso mwa wokondedwa wanga ndili ngati wodzetsa mtendere. Mwamuna
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndine khoma, mawere anga akunga nsanja zake: Pamaso pa mnyamatayo ndinafanana ngati wopeza mtendere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndili ngati khoma, ndipo mawere anga ndi nsanja zake. Tsono mʼmaso mwa bwenzi langa ndine wobweretsa mtendere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndine khoma, maere anga akunga nsanja zace: Pamaso pa mnyamatayo ndinafanana ngati wopeza mtendere.